We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

Ungalape ndi kukhukhulupilira Khristu ndi mphamvu zako?

from Mafunso Ndi Mayankho Vol. 3: Khristu Ndi Ntchito Zake (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

1. Ungalape ndi kukhukhulupilira Khristu ndi mphamvu zako?

Maso anu sanaone makutu sanamve
Palibe amadziwa zomwe Mulungu wakonza
Kwa iwo womkonda
Mulungu wazionetsa kwa ine (*2)

Ungalape ndi kukhulupira Khristu
Ungalape ndi kukhulupira ndi mphamvu zako ungakhulupilire
Mulungu wazionetsa kwa ine

Sitinalandire, mzimu wamdziko
Koma mzimu wa kwa Mulungu
Kuti tidziwe ndikumvetsa zomwe Mulungu watipatsa
Mulungu wandipatsa ulele

1 Akolinto, chaputa 2 ndime 9
Palibe amadziwa zomwe Mulungu wakonza
Kwa iwo omkonda
Mulungu wazionetsa kwa ine
Ayi sinadziwe za chipulumutso changa koma Khristu wazionetsa izi kwa ine

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account