We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

Kodi Mulungu sakondwela ndi omuda komanso osamumvera?

from Mafunso Ndi Mayankho Vol. 4: Mau A Mulungu (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

15. Kodi Mulungu sakondwela ndi omuda komanso osamumvera?

Masalimo chaputala 7:9 mpaka 11(*2)
Atate wa mwamba odziwa iso ndi mtima
Thetsani nkhondo zaoipa nditetezeni
Chida changa ndinu
Mupulumutsa oongoka, oweruza wangwiro
Mumva mkwiyo nthawi zones
Oooooh owuhooooo hoooo
Mulungu sakondwera ndi omuda iye
Amakwiya ndi woipa nthawi zonse
Mulungu sakondwera ndi osamvera?
Amakwiya ndi woipa nthawi zonse
Musang’ambe zovala zanu muchisoni
Koma mitima, bwererani kwa Ambuye
Ngwachifundo, chikondi, wosakwiya nsanga
Ngokhululuka, ali chile kuleza
Yoweli 2:13

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account