We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

Kodi Khristu akhala bwanji Mneneri wako?

from Mafunso Ndi Mayankho Vol. 3: Khristu Ndi Ntchito Zake (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

9. Kodi Khristu akhala bwanji Mneneri wako?

Ndiphuzira chifuniro chake
Khristu andiphuzitsa chifuniro chake

Kuchoka mbuku la Yesaya 61 Khristu anawelenga
Mzimu wa Ambuye uli pa ine
Pakuti wandidzodza ndilalikire kwa osauka
Kumasula a msinga
Osaona kuti aone
Kulimbikitsa ofooka
Kukhazikitsa chaka chokomera Yehova

Ndiphuzira chifuniro chake
Khristu andiphuzitsa chifuniro chake

Khristu ali bwanji mneneri
Yohane 15 :15
Ndiphuzira chifuniro chake
Khristu andiphuzitsa chifuniro chake
Zonse ndaphuzira kwa a tate ndakudziwitsani
Mzimu wa Ambuye ali pa ine
Pakuti wandidzodza ndilalikire kwa osauka
Kumasula msinga

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account