We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

Kodi anthu amapulumuka bwanji Khristu asanabwere?

from Mafunso Ndi Mayankho Vol. 3: Khristu Ndi Ntchito Zake (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

3. Kodi anthu amapulumuka bwanji Khristu asanabwere?

Abelo enoki, Nowa , Abrahamu, Isake, Yakobo, Sara, Yosefe
Makolo a mose, Mose, Lahabe, Gidioni, Barati, Samisoni, Yefita
Davide, Samueli ndi Aneneri

Kuyang’anira ku mzinda
Kufunitsitsa kumwamba

Anthu onsewa anali mchikhulupiliro pakufa
Sanalandire zolonjezedwa, anangoziona patali
Anangoona ndi kuzilandira patali
Kufunitsa ku mwamba

Anthu ankapulumuka bwanji Khristu asanabwere
amkapulumuka pokhulupira
Kukhulupira mpulumutsi
Heberi 11
Kukhulupira mpulumutsi

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account

If you like Songs for Saplings, you may also like: