We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

KHRISTU ADAGWIRA NTCHITO YANJI YOKUPULUMUTSA?

from Mafunso ndi Mayankho Vol. 2: KUGWA NDI CHIPULUMUTSO (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

20. KHRISTU ADAGWIRA NTCHITO YANJI YOKUPULUMUTSA?

Mulungu anamuyesa, iye
Wopanda uchimo kukhala tchimo
Kukhala tchimo m’malo mwathu
Kuti mwa iye tikakhale tikakhale
Chiyero cha Mulungu
Chiyero cha Mulungu
2 Akorinto 5 ndime 21

Khristu adatani populumutsa?
Adasunga malamulo a Mulungu
Nalangidwa chifukwa cha machimo anga
Chifukwa cha machimo anga

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account