We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.
/

lyrics

12. Analemba Baibulo ndi ndani?

Mzakukumbutsani nthawi zones za izi
Ndingakhale m’dziwe muli mchilungamo
Muli maso koma mdzakupatsani kupeza kwa bwino
Kukupatsa mpaka kuchoka msasa omwe ndili nawowo
Uuuuuuuuu uuuuuuuuu uuuuuuuwaaaaa
Ndipo mumvetsere bwino za izi mpaka kuwala mu mdima
Kuwala mu mdima
Ndipo inu mumvetsere bwino za izi mpaka kuwala kwa mawa
Mpaka nyali iwale mu mitima yanu
Uuuuuuuuuuu uuuuuuuu uuuuuuwaaa
Analemba Baibulo anthu a Mulungu
Osankhidwa ndi Mulungu
Analemba Baibulo anthu a Mulungu
Owuzidwa ndi Mzimu oyera
2 Petro 1
Anthu analankula
Monga mwa mzimu oyera

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account